Prières en chewa (chicheŵa)
autorenewChargement de la carte




Vous aimez ce projet? Soutenez le par une donation via PayPal.
Chewa, nyanja (chicheŵa)
face Locuteur: Dominic (Malawi, Lilongwe)
add_circle_outline Église: Église catholique (romaine)
translate Plus d'information sur la langue:
import_contacts Origine du texte: Le texte vient des ressources officielles de l'église.
add_circle_outline Église: Église catholique (romaine)
translate Plus d'information sur la langue:
- Famille des langues: Nigéro-congolaise
- Wikipédia: Chewa, nyanja
- Ethnologue: Chewa, nyanja
import_contacts Origine du texte: Le texte vient des ressources officielles de l'église.
Signe de la Croix en chewa (chicheŵa)
play_circle_filled
Mdzina la Atate, ndi la Mwana ndi la Mzimu Woyera. Amen
Notre Père en chewa (chicheŵa)
play_circle_filled
Atate athu muli m'mwamba,
dzina lanu liyeretsedwe,
ufumu wanu udze,
kufuna kwanu kuchitidwe,
monga kumwamba choncho pansi pano.
Mutipatse ife lero chakudya chathu cha lero.
Mutikhululukire ife zochimwa zathu,
monga ifenso tiakhululukira adani athu,
musatisiye ife m'chinyengo,
koma mutipulumutse ife kwa zoyipa.
Amen
dzina lanu liyeretsedwe,
ufumu wanu udze,
kufuna kwanu kuchitidwe,
monga kumwamba choncho pansi pano.
Mutipatse ife lero chakudya chathu cha lero.
Mutikhululukire ife zochimwa zathu,
monga ifenso tiakhululukira adani athu,
musatisiye ife m'chinyengo,
koma mutipulumutse ife kwa zoyipa.
Amen
Je vous salue Marie en chewa (chicheŵa)
play_circle_filled
Tikuoneni Maria wa chaulele chodzadza,
Ambuye ali nanu.
Ndinu odala kopambana akazi onse,
Ndipo mngodalanso mwana wanu Yesu.
Maria oyera amayi a mulungu
mutipempherere ife ochimwa,
Tsopano ndiponso pa nthawi yakufa kwathu.
Amen
Ambuye ali nanu.
Ndinu odala kopambana akazi onse,
Ndipo mngodalanso mwana wanu Yesu.
Maria oyera amayi a mulungu
mutipempherere ife ochimwa,
Tsopano ndiponso pa nthawi yakufa kwathu.
Amen
Gloire au Père en chewa (chicheŵa)
play_circle_filled
Ulemu ukhale kwa Atate, ndi kwa Mwana ndi kwa Mzimu Woyera,
monga panali poyamba ndi tsopano ndi masiku onse, ndi pa nthawi zosatha.
Amen
monga panali poyamba ndi tsopano ndi masiku onse, ndi pa nthawi zosatha.
Amen
Symbole des Apôtres en chewa (chicheŵa)
play_circle_filled
Ine ndimvera Mulungu Atate wamphamvu zonse,
amene analenga Dziko la kumwamba ndi dziko la pansi pano.
Ndipo Yesu Khristu Mwana wake yekha, Ambuye athu,
amene anayikidwa m'mimba ndi Mzimu Woyera,
nabadwa mwa Maria Virigo,
adamsautsa kwa Ponsio Pilato.
Adampachika pamtanda, anamwalira, adamuyika m'manda,
adalowa m'limbo, ndipo mkuja wake adauka kwa akufa,
nakwera kumwamba nakhala padzanja lamanja la Mulungu Atate Amphamvu zonse.
Adzafumira komweko kudzaweruza amoyo ndi akufa.
Ndipo ndimvera Mzimu Woyera,
Eklezia Katolika Woyera,
ndimveranso kuti Oyera ayanjana,
Mulungu atikhululukira machimo,
thupi lidzauka,
ulipo moyo osatha.
Amen
amene analenga Dziko la kumwamba ndi dziko la pansi pano.
Ndipo Yesu Khristu Mwana wake yekha, Ambuye athu,
amene anayikidwa m'mimba ndi Mzimu Woyera,
nabadwa mwa Maria Virigo,
adamsautsa kwa Ponsio Pilato.
Adampachika pamtanda, anamwalira, adamuyika m'manda,
adalowa m'limbo, ndipo mkuja wake adauka kwa akufa,
nakwera kumwamba nakhala padzanja lamanja la Mulungu Atate Amphamvu zonse.
Adzafumira komweko kudzaweruza amoyo ndi akufa.
Ndipo ndimvera Mzimu Woyera,
Eklezia Katolika Woyera,
ndimveranso kuti Oyera ayanjana,
Mulungu atikhululukira machimo,
thupi lidzauka,
ulipo moyo osatha.
Amen
Vidéos suggérées | Voir plus sur mon canal YouTube
Fraternita Donum Dei - Mala'efo'ou | Singers from Donum Dei fraternity | Travailleuses Missionaires
2013-04-16 Na sopce Mount Yasur 1 | Mt. Yasur volcano